البحث

عبارات مقترحة:

القادر

كلمة (القادر) في اللغة اسم فاعل من القدرة، أو من التقدير، واسم...

الآخر

(الآخِر) كلمة تدل على الترتيب، وهو اسمٌ من أسماء الله الحسنى،...

الرحمن

هذا تعريف باسم الله (الرحمن)، وفيه معناه في اللغة والاصطلاح،...

KUSIYANA KWA AMAYI A CHISILAMU NDI AMAYI A MU CHIKHALIDWE CHA CHIYUDA NDI CHIKHRISTU

الشيشيوا. الشيوا. نيانجا - Chi-Chewa

المؤلف
القسم كتب وأبحاث
النوع نصي
اللغة الشيشيوا. الشيوا. نيانجا - Chi-Chewa
المفردات نوازل الأحوال الشخصية وقضايا المرأة
Buku ili lasonkhanitsa kakhalidwe kwa amayi m’zipembedzo zitatu: Chiyuda, Chikristu ndi Chisilamu. Bukuli lalongosola mfundo zofunikira zochokera mu Chiyuda, komwe mzimayi sanangomutchula kuti ndi wochimwa, koma anatinso ndiyemwe anamuchimwitsa mwamuna. Koma Qur’an ili ndi kuwona kosiyana ndi mabuku ena onse, poti imamuona mzimai kuti ndi wofunikira kwambiri pa chitukuko cha munthu. Kumbali ya kuchimwa kapena kulungama, mzimai ali ndi kakhalidwe kofanana ndi mwamuna mchipembedzo; iye sichiyambi ya machismo onse. Bukuli lalongosola zokhudza Hijaab, ufulu wa kuphunzir kwa mkazi, ufulu wa kukhala ndi chuma chake pambuyo pa kukwatira, kulowa mmalo pambuyo pa kumwalira m’bale wake, mitala ndi nkhani zina. Awerengi a bukuli azindikira kusiyana komwe kulipo pakati pa Chisilamu ndi zipembedzo zina.

المرفقات

2

KUSIYANA KWA AMAYI A CHISILAMU NDI AMAYI A MU CHIKHALIDWE CHA CHIYUDA NDI CHIKHRISTU
KUSIYANA KWA AMAYI A CHISILAMU NDI AMAYI A MU CHIKHALIDWE CHA CHIYUDA NDI CHIKHRISTU